Hon Bonface Kashololo

Hon Bonface Kashololo +265999383825 tsamba ili latsegulidwa kwa inu okonda phwete..awa si malo a ndale,otukwanirapo koma ophwetukirapo kuchotsa nkhawa zanu

Kulira kwaachule sikungaletse Njovu kumwa madziSindikuopa kapena kumunjenjemera aliyense ozunza thupi Ndipo any weapon f...
08/06/2025

Kulira kwaachule sikungaletse Njovu kumwa madzi

Sindikuopa kapena kumunjenjemera aliyense ozunza thupi

Ndipo any weapon formed against me shall not prosper
Or Mundisemere izi ndi izi pamapeto pazonse mzapezekedi kuti ndinu olephera

Mulungu amene ndimamupembeza ine ndi oyankha ndipo pompano muyankhidwa.

Bonface Kashololo36 simundimaliza inu musanathe psitiiiiii

Mawa tili busy
04/04/2025

Mawa tili busy

TIKAMAYANKHULA NDE WINA AZITI BOMA NDILOMWELIAkati apange mademo akwezeledwe malipiro mmawatumira anyamata azikwanje.MPH...
04/04/2025

TIKAMAYANKHULA NDE WINA AZITI BOMA NDILOMWELI

Akati apange mademo akwezeledwe malipiro mmawatumira anyamata azikwanje.

MPHUZITSI WAZIPHA KAMBA KA MALUZI

Mphunzitsi wina yemwe amaphunzitsa pa Milonde Primary School mdela la Mitundu, ku Lilongwe, wazipha pozimangilira.

Dzina la mphunzitsiyu ndi John Mwalilino.Asanaziphe,analemba kalata ili mmusiyi kuti ndalama zake zikatuluka zigawidwe kwa ana ake komanso abweze ngongole kwa omwe anawangongolera. Maliro apita ku Karonga komwe akayikidwe.

MALAWI NEWS FLASH
πŸ‡²πŸ‡ΌπŸ‡²πŸ‡ΌπŸ‡²πŸ‡Ό

04/04/2025

Pochoka m'boma pa 16 September 2025
Chilichonse azakhala kuti abamo m'boma

Izi ndi mbava sono umbava wasefukira mpaka kumasapota awo woooooo

Mwabazo zakwana sitilora ndipo sitizalora kuti pa 16 September 2025 mzabere mavote
Ndipo msayelekeze kulingalira zobera chomwe mngapange yambani kupakira kunyumba yabomako chifukwa kukubwera mwini wake odziwa kulamula dziko ndi zofuna amalawi

Inu mmangodziwa kuba basiiiiiii

MCP NEVER AGAIN

04/04/2025

Uthenga waulere uwu

21/10/2024

LANGIZO LANGA LA ULERE KWA INU A MCP

Kuchoka mu 2020 kufika lero 2024 pamene MCP ikulamula boma
Zinthu zambiri zaonongeka ndipo palibe chimene chikuyenda bwino mdziko lino.

Tibwelere mmbuyo pang'ono chipani cha MCP chinalonjeza anthu kuti Feteleza azizagula motchipa pamtengo wa k4500 osati zamakuponi . Mnthawi imeneyo feteleza ankagulitsidwa pamtengo wa k18,000 ndipo ogula kwambiri unali pa k22,000 pamene wamakuponi umagulitsidwa pamtengo wa k4500.
Anthu analonjezedwa kuti madzi komanso magetsi azizaitanitsa ulere
Nthawi imeneyo cement ankagulitsidwa pamtengo wa k5000. Pamene sugar unali pa k600 nthawi imeneyo Sopo tinkagula wochapira k50 mafuta agalimoto anali pa k630.

MCP inaonetsa kuti ichita zinthu mmalawi muno ndipo amalawi onse anaika chikhulupiliro pa MCP.
Koma MCP zimene yaapanga amalawi pa zaka 4 izi amalawi atayiratu chiyembekezo ndi MCP ndipo sakufunanso kumva dzina la MCP.
MCP yaapanga amalawi kukhala anthu ozunzika kwambiri, yaawonetsa zibalo mudziko lawo lomwe akumva kuwawa palibe chikuyenda. Ndipo pano amalawi akuyenda olutsa lutsa chifukwa ambiri ma business awo anagwa, ena ntchito anachotsedwa, ena ananamizidwa kuti azawalemba ntchito anthu 1 million zomwe sizinatheke.

Ili ndi boma la bodza , lakatangale komanso la nkhanza chimene limadziwa boma ili ndi chipani cha MCP ndikumanga anthu basi.
Inu amene mkuimira chipani cha MCP 2025 musamale kwambiri chifukwa tikayang'ana pa ground apa kuchipani cha MCP sizilibwino. Anthu sakuyifuna or dontho msapusitsidwe ndimisonkho akumapanga a MCP anthu aja akumachita kuwagula aliyense akumapatsidwa t-shirt ndi k2000 kumanja kuti abwere kumsonkhano wawo.

Pangani chisankho chabwino nthawi isanathe kuli bwino muime panokha ngati simukuzifuna zipani zinazi. MCP amalawi sakuyifuna or pang'ono ndipo yaapangitsa amalawi ambiri kuzipha chifukwa cha mavuto osiyana siyana amene chapanga mdziko lino. MCP yaapanga amalawi kukhala osaukisitsa kwambiri. 2025 anthu sazaivotera MCP olira achuluka, amene akuimira pa tiketi ya MCP asamale kwambiri ndipo aganize kawiri katatu anthu ndiokwiya mmamidzi umu. Voti ya chaka cha mawa ndiya chikuwawe.

Malangizo anga awulere awa zili kwainu kugwilitsa ntchito nthawi isanathe.

27/09/2024

Mkati mwaulendo wakukenani

Koma nde muli zinthu zolemera

27/09/2024

Nothing is more fulfilling than supporting a party that delivers.

join the DPP! love APM, our great Leader.

Okafufuza page ya Mikozi
25/09/2024

Okafufuza page ya Mikozi

25/09/2024

Mikozi walowa MCP koma sanafune kuti muchite kupanga unfollow
Wangodeletilatu page yonse kukana za Dan Lu

Kodi Inu mwapanga kale unfollow? Ku page ya Dan Lu Kapangen mwachangu changu mutsanatsaleko nokha
24/09/2024

Kodi Inu mwapanga kale unfollow? Ku page ya Dan Lu Kapangen mwachangu changu mutsanatsaleko nokha

24/09/2024

Nde kuli unfollow Dan Lu page campaign
Amalawi si opusa amuonetsa chimene Ali Dan Lu nane ndapanga unfollow

Address

Kawali
Lilongwe

Telephone

+265999383825

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Hon Bonface Kashololo posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share